top of page
Search

Ana 1 Miliyoni Kupemphera Kolona mu Dinale ya Maula

Ana a Tilitonse ochokera ku Maula Cathedral apemphera nawo Kolona wa Ana okwana 1 million ku Parish ya St. Dennis Ssebbugwawo - Chinsapo mu Arkidayosizi ya Lilongwe.


Chaka ndi chaka ana okwana 1Million pa dziko lonse la pansi amapephera kolona.


Kolona amapepheredwa pa 18 October koma chaka chino kolonayi wapepheredwa pa 7 October kamba koti ndi tsiku lomwe lidayamba kupempheredwa mchaka cha 2005 zomwe zikutanthauza kuti papita zaka 20 chiyambireni kupempheredwa.


Mwana wochokera ku Maula Cathedral, Thokozile Soko anawerenga ndi kutsogolera khumi lachiwiri.

Thokozile Soko kuwerenga ndi kutsogolera khumi lachiwiri
Thokozile Soko kuwerenga ndi kutsogolera khumi lachiwiri

 
 
 

Comments


ABOUT US

We are simply known as a Cathedral of Lilongwe, which is the Capital City of Malawi. We belong to the metropolitan Archdiocese of Lilongwe whose safragan dioceses are Dedza, Mzuzu and Karonga. We follow the Roman or Latin rite.

ADDRESS

+265 (0) 1 755 846

+265 (0) 998 73 35 93

P.O Box 1524, Lilongwe.

info@maulaparish.org

louis2chikanya@gmail.com

SUBSCRIBE FOR EMAILS

Thanks for submitting!

  • Facebook
  • Instagram
  • Twitter

© 2025 by Team iWork. Proudly created with Wix.com

bottom of page