top of page
Search

Bungwe la Amayi aChikatolika kutsogolera chipembedzo m'chaka cha tsopano


Pamene chaka cha 2026 chayamba kumene, mabungwe komanso miphakati ya parishi ya Maula, yakangalika kupanga mapologalamu ofuna kuti atumikire ikafika nthawi yawo.


Nthawi ndi nthawi mabungwe komnaso miphakati imene ili pa parishiyi imatenga gawo pakutsogolera chipembedzo.


Limodzi mwa mabungwe omwe ayenditsa kale chipembedzo mchakachi ndi bungwe la amayi achiKatolika la CWA.


Loweruka pa 17 January 2026, amayiwa anakoza mu tchalitchi komanso kusamala malo ena.


Amayiwa sanalekere pomwepo ayi, tsiku la Mulungu anapereka mphatso za paguwa komaso kuwerenga mau.



Parishi ya Maula ndiyothokoza bungwe la amayi achiKatolikawa kamba kotsogolera chipembedzo.

 
 
 

Comments


ABOUT US

We are simply known as a Cathedral of Lilongwe, which is the Capital City of Malawi. We belong to the metropolitan Archdiocese of Lilongwe whose safragan dioceses are Dedza, Mzuzu and Karonga. We follow the Roman or Latin rite.

ADDRESS

+265 (0) 1 755 846

+265 (0) 998 73 35 93

P.O Box 1524, Lilongwe.

info@maulaparish.org

louis2chikanya@gmail.com

SUBSCRIBE FOR EMAILS

Thanks for submitting!

  • Facebook
  • Instagram
  • Twitter

© 2025 by Team iWork. Proudly created with Wix.com

bottom of page