top of page
Search

Sukulu ya Mlale Minor Seminale iyendera Parish ya Maula


Ophunzira ochokera ku sukulu ya St. Paul Minor Seminary - Mlale mu Arkidayosozi ino ya Lilongwe alimbikitsidwa kukhala okonda maphunziro awo.


Izi zayankhulidwa ndi a Chapola, omwe ndi wapampando wa akhristu omwe amapephera Misa ya Latin ku Maula Cathedral.


A Chapola ati ali ndi chiyembekezo kut ena mwa anyamatawa adzakhala ansembe, poti munda wakula achepa ndi ntchito.


"Inu achinyamata limbikirani maphunziro anu kut ena mwa inu mudzatumikire Mulungu.


Ndipo bambo Peter Makina anathokoza ophunzirawa chifukwa chodzapemphera nawo ku Maula Cathedral.


Ophunzirawa anapemphera ndi kuyimbira pa mwambo wa nsembe ya Misa ya Latin ku Maula, ndipopamapeto pa nzonse iwo anacheza ndikudyera pamodzi ndi akhristu ngati banja limodzi.


Misa ya Latin ku Maula Cathedral imakhalapo kamodzi Lamulungu loyamba la mwezi uli onse.

 
 
 

Comments


ABOUT US

We are simply known as a Cathedral of Lilongwe, which is the Capital City of Malawi. We belong to the metropolitan Archdiocese of Lilongwe whose safragan dioceses are Dedza, Mzuzu and Karonga. We follow the Roman or Latin rite.

ADDRESS

+265 (0) 1 755 846

+265 (0) 998 73 35 93

P.O Box 1524, Lilongwe.

parishpriest@maulaparish.org

administration@maulaparish.org

SUBSCRIBE FOR EMAILS

Thanks for submitting!

  • Facebook
  • Instagram
  • Twitter

© 2025 by Team iWork. Proudly created with Wix.com

bottom of page